Quantcast
Channel: Health | Malawi Nyasa Times - News from Malawi about Malawi
Viewing all articles
Browse latest Browse all 2462

Wapolisi azipha poziponya munsinje kamba ka chibwezi

$
0
0

  Wapolisi wina ku Rumphi wadziponya mu mtsinje wa South Rukulu omwe pano wadzadza ndikusefukira mbali zina m’bomali. Mneneri wa polisi mchigawo chakumpoto a Maurice Chapola, angotsimikiza zoti alandira lipoti lakusowa kwa a Ngamanya Mbale koma anakana kuyankhulapo zambiri ponena kuti kafukufuku wawo ali mkati. Koma yemwe watitsina khutu wati a Mbale adziponya mu mtsinjewu […]

The post Wapolisi azipha poziponya munsinje kamba ka chibwezi appeared first on Malawi Nyasa Times - News from Malawi about Malawi.

Viewing all articles
Browse latest Browse all 2462

Trending Articles



<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>